‘Therefore let us leave the elementary doctrine of Christ and go on to maturity, not laying again a foundation of repentance from dead works and of faith toward God, and of instruction about washings, the laying on of hands, the resurrection of the dead, and eternal judgment.’ (Hebrews 6:1-2, ESV)
This booklet explains the foundations of our Christian faith and what this means for us as believers. It also highlights where these truths can be found in Scripture.
Maziko a Chikhulupiliro
CHIPANGIZO CHAPAMWAMBA CHA UKHULUPILIRA ATSOPANO
Ahebri 6:1-2 limanena kuti, ‘Tsono tisangoima pa maphunziro oyamba enieni a Khristu. Tisachite kubwerezanso kuphunzitsa zomwe zili ngati maziko, monga za kutembenuka mtima kusiya ntchito zosapindululitsa moyo wosatha, za kukhulupirira Mulungu, za maubatizo, za kusanjika manja, za kuuka kwa akufa, ndi za chiweruzo chotsiriza. Koma tiyeni tipitirire mpaka tikafike pa kukhwima kwenikweni.’
This booklet was translated by: Andrew Kapalula Junior